Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 42:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Moyo wanga ukulakalaka Mulungu,+ ukulakalaka Mulungu wamoyo.+

      Ndidzapita liti kunyumba ya Mulungu kukaonekera pamaso pake?+

  • Salimo 84:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Ndimalakalaka mabwalo a Yehova ndipo ndafookeratu chifukwa cholakalaka mabwalowo.+

      Mtima wanga ndi thupi langa zikufuula mosangalala kwa Mulungu wamoyo.+

  • Yesaya 26:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Usiku, mtima wanga umakulakalakani.+ Ndithu ndimakufunafunani ndi mtima wonse,+ chifukwa mukadzaweruza dziko lapansi,+ anthu okhala panthaka ya dzikolo adzaphunzira chilungamo.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena