Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 10:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Dzombelo linakuta nthaka yonse ya m’dzikolo+ ndipo dziko linachita mdima.+ Dzombelo linadya zomera zonse za m’dzikolo ndi zipatso zonse za m’mitengo zimene sizinawonongeke ndi matalala,+ moti sipanatsale chobiriwira chilichonse m’mitengo kapena pa zomera m’dziko lonse la Iguputo.+

  • Salimo 105:34
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 34 Analamula kuti pagwe dzombe,+

      Ndipo panagwa dzombe losawerengeka la mtundu winawake.+

  • Amosi 7:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, anandionetsa masomphenya awa: Ndinamuona akutumiza dzombe, anthu atatsala pang’ono kubzala mbewu zomaliza.+ Nthawi imeneyi inali yobzala mbewu zomaliza, anthu atamweta udzu wopita kwa mfumu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena