Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 10:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Pomwepo Mose analoza dziko lonse la Iguputo ndi ndodo yake, ndipo Yehova anachititsa mphepo yochokera kum’mawa+ kuwomba padziko lonselo, usana wonse ndi usiku wonse. M’mawa kutacha mphepoyo inabweretsa dzombe.

  • Deuteronomo 28:38
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 38 “Udzapita ndi mbewu zambiri kumunda, koma udzakolola zochepa+ chifukwa dzombe lidzadya mbewuzo.+

  • Salimo 78:46
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 46 Anapereka zokolola zawo kwa mphemvu,

      Ndipo ntchito yawo yolemetsa anaipereka kwa dzombe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena