Genesis 41:6 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 6 Anaonanso ngala zina 7 zikutuluka pambuyo pa zoyambazo.+ Ngalazo zinali zonyala ndi zowauka ndi mphepo yakum’mawa.+ Ekisodo 14:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 Tsopano Mose anatambasula dzanja lake kuloza panyanja,+ ndipo Yehova anachititsa mphepo yamphamvu yakum’mawa kuyamba kugawa nyanjayo usiku wonse ndi kuumitsa pansi pake.+ Motero madziwo anali kugawikana.+ Salimo 78:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Anachititsa mphepo ya kum’mawa kuwomba m’mlengalenga,+Ndipo mwa mphamvu zake anachititsa mphepo ya kum’mwera kuwomba.+ Yona 4:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Dzuwa litatuluka, Mulungu anatumiza mphepo yotentha yochokera kum’mawa.+ Dzuwalo linamutentha Yona pamutu moti anangotsala pang’ono kukomoka.+ Choncho Yona anapempha mobwerezabwereza kuti angofa. Iye anali kunena kuti: “Kuli bwino ndife kusiyana n’kuti ndikhale ndi moyo.”+
6 Anaonanso ngala zina 7 zikutuluka pambuyo pa zoyambazo.+ Ngalazo zinali zonyala ndi zowauka ndi mphepo yakum’mawa.+
21 Tsopano Mose anatambasula dzanja lake kuloza panyanja,+ ndipo Yehova anachititsa mphepo yamphamvu yakum’mawa kuyamba kugawa nyanjayo usiku wonse ndi kuumitsa pansi pake.+ Motero madziwo anali kugawikana.+
26 Anachititsa mphepo ya kum’mawa kuwomba m’mlengalenga,+Ndipo mwa mphamvu zake anachititsa mphepo ya kum’mwera kuwomba.+
8 Dzuwa litatuluka, Mulungu anatumiza mphepo yotentha yochokera kum’mawa.+ Dzuwalo linamutentha Yona pamutu moti anangotsala pang’ono kukomoka.+ Choncho Yona anapempha mobwerezabwereza kuti angofa. Iye anali kunena kuti: “Kuli bwino ndife kusiyana n’kuti ndikhale ndi moyo.”+