Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 8:36
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 36 inuyo mumve muli kumwamba ndipo mukhululuke tchimo la atumiki anu, anthu anu Aisiraeli, popeza mumawaphunzitsa+ njira yabwino yoti ayendemo.+ Mubweretse mvula+ padziko lanu, limene mwapatsa anthu anu monga cholowa.

  • Salimo 27:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Ndilangizeni, inu Yehova, kuti ndiyende m’njira yanu.+

      Nditsogolereni m’njira yowongoka kuti nditetezeke kwa adani anga.

  • Salimo 119:33
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  33 Ndilangizeni inu Yehova, kuti ndiyende motsatira malangizo anu,+

      Kuti nditsatire malangizo anu moyo wanga wonse.+

  • Salimo 143:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 M’mawa ndichititseni kumva za kukoma mtima kwanu kosatha,+

      Pakuti ndimadalira inu.+

      Ndidziwitseni njira imene ndiyenera kuyendamo,+

      Pakuti ndapereka moyo wanga kwa inu.+

  • Yesaya 54:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ana ako onse+ adzakhala anthu ophunzitsidwa ndi Yehova,+ ndipo mtendere wa ana ako udzakhala wochuluka.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena