Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 30:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Chifukwa mkwiyo wa Mulungu sukhalitsa pa munthu,+

      Koma kukoma mtima kwake ndi kwa moyo wonse.+

      Usiku kumakhala kulira,+ koma m’mawa kumakhala kufuula ndi chisangalalo.+

  • Salimo 126:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Amene akukhetsa misozi pofesa mbewu,+

      Adzakolola akufuula mosangalala.+

  • Mateyu 5:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 4 “Odala ndi anthu amene akumva chisoni, chifukwa adzasangalatsidwa.+

  • Yohane 16:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndithudi ndikukuuzani, Mudzagwetsa misozi ndi kulira mofuula, koma dzikoli lidzasangalala. Mudzamva chisoni,+ koma chisoni chanu adzachisandutsa chimwemwe.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena