Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 68:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Mulungu wanu walamula mphamvu zanu kuti zionekere.+

      Inu Mulungu, sonyezani mphamvu monga mmene mwachitira kwa ife.+

  • Salimo 118:25
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 25 Haa! Inu Yehova, chonde tipulumutseni.+

      Haa! Inu Yehova, chonde tithandizeni kuti zinthu zitiyendere bwino.+

  • Yesaya 26:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Inu Yehova, mudzachita chilungamo kuti mutipatse mtendere,+ pakuti ntchito zathu zonse tazikwanitsa chifukwa cha inu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena