Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 49:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Pakuti amaona kuti ngakhale anthu anzeru amafa,+

      Wopusa ndi wopanda nzeru, onsewo amawonongeka,+

      Ndipo chuma chawo amasiyira anthu ena.+

  • Salimo 73:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ndinakhala wopanda nzeru ndipo sindinadziwe kanthu.+

      Ndinakhala ngati nyama yakuthengo pamaso panu.+

  • Salimo 92:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Munthu wopanda nzeru sangadziwe zimenezi,+

      Ndipo munthu wopusa sangazimvetse.+

  • Miyambo 12:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Wokonda malangizo* amakondanso kudziwa zinthu,+ koma wodana ndi chidzudzulo ndi wopanda nzeru.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena