1 Mbiri 16:26 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 26 Chifukwa milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi milungu yopanda pake.+Koma Yehova, ndiye anapanga kumwamba.+ Salimo 97:7 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 7 Onse amene akupembedza chifaniziro chilichonse achite manyazi.+Amene amadzitama chifukwa cha milungu yopanda pake achite manyazi.+Muweramireni, inu milungu yonse.+ Yesaya 37:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Atentha milungu yawo pamoto,+ chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga.+ Yesaya 44:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 Kwa aliyense amene wapanga mulungu kapena kuumba fano lopangidwa ndi chitsulo chosungunula,+ lidzakhala lopanda phindu ngakhale pang’ono.+ Yeremiya 10:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Mitunduyo mukaiuze izi anthu inu: “Milungu+ imene sinapange kumwamba ndi dziko lapansi+ ndi imene idzawonongedwe padziko lapansi, pansi pa thambo.” 1 Akorinto 8:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Ndiyeno pa nkhani ya kudya+ zakudya zoperekedwa kwa mafano, timadziwa kuti fano ndi lopanda pake+ m’dziko, ndiponso kuti kulibe Mulungu wina koma mmodzi yekha.+
26 Chifukwa milungu yonse ya anthu a mitundu ina ndi milungu yopanda pake.+Koma Yehova, ndiye anapanga kumwamba.+
7 Onse amene akupembedza chifaniziro chilichonse achite manyazi.+Amene amadzitama chifukwa cha milungu yopanda pake achite manyazi.+Muweramireni, inu milungu yonse.+
19 Atentha milungu yawo pamoto,+ chifukwa sinali milungu,+ koma ntchito ya manja a anthu,+ mitengo ndi miyala, n’chifukwa chake anaiwononga.+
10 Kwa aliyense amene wapanga mulungu kapena kuumba fano lopangidwa ndi chitsulo chosungunula,+ lidzakhala lopanda phindu ngakhale pang’ono.+
11 Mitunduyo mukaiuze izi anthu inu: “Milungu+ imene sinapange kumwamba ndi dziko lapansi+ ndi imene idzawonongedwe padziko lapansi, pansi pa thambo.”
4 Ndiyeno pa nkhani ya kudya+ zakudya zoperekedwa kwa mafano, timadziwa kuti fano ndi lopanda pake+ m’dziko, ndiponso kuti kulibe Mulungu wina koma mmodzi yekha.+