Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 27:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 “Inu Yehova, Mulungu wa miyoyo ya zamoyo+ zamitundu yonse,+ sankhani munthu woti aziyang’anira khamuli.+

  • Yobu 33:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Mzimu wa Mulungu unandiumba,+

      Mpweya wa Wamphamvuyonse unandipatsa moyo.+

  • Salimo 33:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  6 Kumwamba kunalengedwa ndi mawu a Yehova,+

      Ndipo makamu ake onse analengedwa ndi mpweya wa m’kamwa mwake.+

  • Yesaya 32:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 kufikira mzimu utatsanulidwa pa ife kuchokera kumwamba,+ ndiponso chipululu chitakhala munda wa zipatso. Munda wa zipatsowo udzakhala ngati nkhalango yeniyeni.+

  • Ezekieli 37:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Tsopano anandiuza kuti: “Losera kwa mphepo. Iwe mwana wa munthu, losera ndipo uuze mphepoyo kuti, ‘Yehova, Ambuye Wamkulu Koposa, wanena kuti: “Iwe mphepo! Bwera kuchokera kumbali zonse zinayi ndi kuwomba anthu ophedwawa+ kuti akhalenso ndi moyo.”’”+

  • Machitidwe 17:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Pakuti chifukwa cha iye tili ndi moyo, timayenda ndipo tilipo,+ monga mmene andakatulo+ ena pakati panu anenera kuti, ‘Pakuti ndife mbadwa zake.’

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena