Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 15:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mphamvu ndi nyonga yanga ndi Ya,*+ pakuti wandipulumutsa.+

      Ameneyu ndi Mulungu wanga, ndidzam’tamanda.+ Ndiye Mulungu wa atate anga,+ ndidzam’kweza.+

  • Salimo 33:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Fuulani mosangalala chifukwa cha Yehova, inu nonse olungama.+

      M’poyenera kuti owongoka mtima atamande Mulungu.+

  • Salimo 118:28
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 28 Inu ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakutamandani.+

      Ndinu Mulungu wanga, ndipo ndidzakukwezani.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena