Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 33:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 33 Fuulani mosangalala chifukwa cha Yehova, inu nonse olungama.+

      M’poyenera kuti owongoka mtima atamande Mulungu.+

  • Salimo 103:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Tamandani Yehova inu makamu ake onse,+

      Inu atumiki ake onse ochita chifuniro chake.+

  • Aefeso 5:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Mukakhala pakati panu muziimba masalimo,+ nyimbo zotamanda+ Mulungu, ndiponso nyimbo zauzimu. Muziimba+ nyimbo zotamanda+ Yehova m’mitima mwanu,

  • Chivumbulutso 19:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Komanso, kunamveka mawu ochokera kumpando wachifumu akuti: “Muzitamanda Mulungu wathu, inu nonse akapolo+ ake, inu omuopa, olemekezeka ndi onyozeka omwe.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena