Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 9:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Koma ndakusiya ndi moyo+ kuti ndikusonyeze mphamvu zanga, ndi kuti dzina langa lilengezedwe padziko lonse lapansi.+

  • Salimo 72:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Lidalitsike dzina lake laulemerero mpaka kalekale,+

      Ndipo ulemerero wake udzaze dziko lonse lapansi.+

      Ame! Ame!*

  • Salimo 86:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Mitundu yonse imene munapanga idzabwera kwa inu,+

      Ndipo idzagwada pamaso panu, inu Yehova,+

      Ndi kulemekeza dzina lanu.+

  • Malaki 1:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 “Kuchokera kotulukira dzuwa kukafika kumene limalowera, dzina langa lidzakwezeka pakati pa anthu a mitundu ina.+ Kulikonse anthu azidzapereka nsembe zautsi.+ Anthu azidzapereka zopereka kapena kuti mphatso zovomerezeka polemekeza dzina langa.+ Adzachita izi chifukwa dzina langa lidzakhala lokwezeka pakati pa anthu a mitundu ina,”+ watero Yehova wa makamu.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena