-
1 Mbiri 16:24Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
24 Fotokozani za ulemerero wake pakati pa anthu a mitundu ina,
Ndiponso za ntchito zake zodabwitsa pakati pa mitundu yonse ya anthu.
-
-
Malaki 1:11Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
11 “Kuchokera kotulukira dzuwa kukafika kumene limalowera, dzina langa lidzakwezeka pakati pa anthu a mitundu ina.+ Kulikonse anthu azidzapereka nsembe zautsi.+ Anthu azidzapereka zopereka kapena kuti mphatso zovomerezeka polemekeza dzina langa.+ Adzachita izi chifukwa dzina langa lidzakhala lokwezeka pakati pa anthu a mitundu ina,”+ watero Yehova wa makamu.
-