Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 19:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Chilamulo+ cha Yehova ndi changwiro,+ chimabwezeretsa moyo.+

      Zikumbutso+ za Yehova ndi zodalirika,+ zimapatsa nzeru munthu wosadziwa zinthu.+

  • Salimo 119:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 119 Odala ndi anthu osalakwitsa kanthu m’njira zawo,+

      Anthu amene akutsatira chilamulo cha Yehova.+

  • Salimo 119:142
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 142 Chilungamo chanu ndi chilungamo mpaka kalekale,+

      Ndipo chilamulo chanu ndi choonadi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena