Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Numeri 23:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Palibe amene walodza Yakobo,+

      Ngakhale kuchesa Isiraeli.+

      Za Yakobo ndi Isiraeli, adzati,

      ‘Mwaonatu zimene Mulungu wachita!’+

  • Yoswa 2:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Ndipo iye anauza amunawo kuti: “Ndikudziwa kuti Yehova akupatsani ndithu dziko lino.+ Ife tagwidwa ndi mantha chifukwa cha inu,+ ndipo anthu a dziko lino ataya mtima chifukwa chokuopani.+

  • Nehemiya 6:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Ndiyeno adani athu onse atangomva zimenezi,+ komanso anthu a mitundu ina yotizungulira ataona, anachita manyazi ndipo anadziwa kuti ntchito imeneyi yatheka chifukwa cha Mulungu wathu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena