Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Oweruza 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Anayamba kusankha milungu yatsopano.+

      Atatero m’pamene nkhondo inafika m’mizinda.+

      Panalibe chishango kapena mkondo waung’ono,

      Pakati pa anthu 40,000 mu Isiraeli.+

  • Salimo 121:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Yehova akukuyang’anira.+

      Yehova ndiye mthunzi wako+ kudzanja lako lamanja.+

  • Yesaya 27:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Ine Yehova ndine mlonda wa mundawo.+ Ndizidzauthirira nthawi zonse.+ Ndizidzaulondera usana ndi usiku kuti wina aliyense asauwononge.+

  • Zekariya 2:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ine ndidzamuzungulira ngati mpanda wake wamoto+ ndipo ndidzamudzaza ndi ulemerero wanga,”’ watero Yehova.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena