Maliro 1:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Yuda wakhala kapolo chifukwa cha nsautso+ ndiponso chifukwa cha kukula kwa ntchito yaukapolo imene akugwira.+Iye wakhala pakati pa mitundu ina ya anthu,+ ndipo sanapeze malo ampumulo.Onse amene anali kumuzunza amupeza pa nthawi ya mavuto ake.+ Ezekieli 23:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Akazi amenewa anayamba kuchita uhule m’dziko la Iguputo.+ Anayamba uhule umenewu ali atsikana ang’onoang’ono.+ Kumeneko amuna anafinya mabere awo+ ndi kutsamira chifuwa chawo ali anamwali. Hoseya 11:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 “Pa nthawi imene Isiraeli anali mnyamata ndinamukonda,+ ndipo ndinaitana mwana wangayu kuti atuluke mu Iguputo.+
3 Yuda wakhala kapolo chifukwa cha nsautso+ ndiponso chifukwa cha kukula kwa ntchito yaukapolo imene akugwira.+Iye wakhala pakati pa mitundu ina ya anthu,+ ndipo sanapeze malo ampumulo.Onse amene anali kumuzunza amupeza pa nthawi ya mavuto ake.+
3 Akazi amenewa anayamba kuchita uhule m’dziko la Iguputo.+ Anayamba uhule umenewu ali atsikana ang’onoang’ono.+ Kumeneko amuna anafinya mabere awo+ ndi kutsamira chifuwa chawo ali anamwali.
11 “Pa nthawi imene Isiraeli anali mnyamata ndinamukonda,+ ndipo ndinaitana mwana wangayu kuti atuluke mu Iguputo.+