Genesis 13:8 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 8 Chotero Abulamu anauza Loti+ kuti: “Chonde, pasakhale mkangano uliwonse pakati pa ine ndi iwe, ndi pakati pa abusa anga ndi abusa ako, pajatu ndife pachibale.+ Genesis 45:24 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 24 Atatero, anauza abale akewo kuti anyamuke, ndipo iwo ananyamuka. Koma anawachenjeza kuti: “Musakanganetu m’njira.”+ Yohane 13:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Mwakutero, onse adzadziwa kuti ndinu ophunzira anga, ngati mukukondana.”+ Yohane 17:21 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 21 kuti onsewa akhale amodzi,+ mmene inu Atate ndi ine tilili ogwirizana,+ kuti iwonso akhale ogwirizana ndi ife,+ ndi kuti dziko likhulupirire kuti inu munanditumadi.+ Akolose 3:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Koma kuwonjezera pa zonsezi, valani chikondi,+ pakuti chimagwirizanitsa anthu mwamphamvu+ kwambiri kuposa chinthu china chilichonse. Aheberi 13:1 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Mupitirize kukonda abale.+
8 Chotero Abulamu anauza Loti+ kuti: “Chonde, pasakhale mkangano uliwonse pakati pa ine ndi iwe, ndi pakati pa abusa anga ndi abusa ako, pajatu ndife pachibale.+
24 Atatero, anauza abale akewo kuti anyamuke, ndipo iwo ananyamuka. Koma anawachenjeza kuti: “Musakanganetu m’njira.”+
21 kuti onsewa akhale amodzi,+ mmene inu Atate ndi ine tilili ogwirizana,+ kuti iwonso akhale ogwirizana ndi ife,+ ndi kuti dziko likhulupirire kuti inu munanditumadi.+
14 Koma kuwonjezera pa zonsezi, valani chikondi,+ pakuti chimagwirizanitsa anthu mwamphamvu+ kwambiri kuposa chinthu china chilichonse.