Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Esitere 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Choncho anapachika Hamani pamtengo+ umene anakonzera Moredekai,+ ndipo mkwiyo wa mfumu unatha.

  • Salimo 94:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Iye adzawabwezera zoipa zawo,+

      Ndipo adzawakhalitsa chete mwa kuwadzetsera masoka okonza okha.+

      Yehova Mulungu wathu adzawakhalitsa chete.+

  • Miyambo 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Munthu woipa amakodwa ndi kuchimwa kwa milomo yake,+ koma wolungama amachoka m’masautso.+

  • Miyambo 18:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Pakamwa pa munthu wopusa m’pamene pamamuwononga,+ ndipo milomo yake ndi msampha wa moyo wake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena