Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 140:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Anthu odzikweza anditchera msampha.+

      Iwo aika zingwe ponseponse ngati ukonde m’mphepete mwa njira,+

      Ndipo anditchera makhwekhwe.+ [Seʹlah.]

  • Yeremiya 18:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 M’nyumba zawo mumveke kulira mukawabweretsera magulu achifwamba mwadzidzidzi,+ chifukwa andikumbira mbuna kuti andigwire ndipo anditchera misampha kuti akole mapazi anga.+

  • Mateyu 22:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Pamenepo Afarisi anachoka ndi kukapangana kuti am’kole m’mawu ake.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena