Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 5:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  8 Inu Yehova, nditsogolereni m’chilungamo chanu+ chifukwa adani anga andizungulira.+

      Salazani njira yanu kuti ndiyendemo popanda chopunthwitsa.+

  • Salimo 31:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Pakuti inu ndinu thanthwe langa ndi malo anga achitetezo.+

      Chifukwa cha dzina lanu+ mudzanditsogolera ndi kundilozera njira.+

  • Miyambo 8:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ndimayenda m’njira yachilungamo,+ komanso pakati pamisewu yachilungamo,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena