Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 10:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Ndisanapite. Ndikapita sindibweranso,+

      Ndikapita kudziko lamdima wandiweyani,+

  • Yobu 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kodi anakuvundukulira zipata za imfa,+

      Kapena zipata za mdima wandiweyani,+ kodi ungathe kuziona?

  • Salimo 44:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pakuti inu mwatiphwanya kumalo amene mimbulu imasonkhana,+

      Mwatiphimba ndi mdima wandiweyani.+

  • Mateyu 4:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 anthu okhala mu mdima+ anaona kuwala kwakukulu,+ ndipo anthu okhala m’dera la mthunzi wa imfa, kuwala+ kunawatulukira.”+

  • Luka 1:79
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 79 ndipo kudzaunikira amene akhala mu mdima ndi mu mthunzi wa imfa,+ ndi kutsogolera bwinobwino mapazi athu panjira yamtendere.”

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena