Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 9:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Ndikomereni mtima inu Yehova. Onani mmene anthu odana nane akundisautsira,+

      Inu Mulungu amene mukundinyamula kundichotsa pazipata za imfa.+

  • Salimo 107:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Moyo wawo unaipidwa ndi chakudya cha mtundu uliwonse,+

      Ndipo anafika pazipata za imfa.+

  • Mateyu 16:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Chotero inenso ndikukuuza kuti, Iwe ndiwe Petulo,+ ndipo pathanthwe+ ili ndidzamangapo mpingo wanga. Zipata za Manda+ sizidzaugonjetsa.+

  • Chivumbulutso 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena