Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 2 Samueli 22:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Pakuti mafunde akupha anandizungulira.+

      Panali chikhamu cha anthu opanda pake amene anali kundiopseza.+

  • Yobu 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kodi anakuvundukulira zipata za imfa,+

      Kapena zipata za mdima wandiweyani,+ kodi ungathe kuziona?

  • Salimo 30:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, mwanditulutsa m’Manda,+

      Mwandisunga ndi moyo, kuti ndisatsikire m’dzenje.+

  • Salimo 107:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Moyo wawo unaipidwa ndi chakudya cha mtundu uliwonse,+

      Ndipo anafika pazipata za imfa.+

  • Salimo 116:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Zingwe za imfa zinandizungulira+

      Ndipo ndinasautsika ngati kuti ndili m’Manda.+

      Ndinapitiriza kusautsika ndi kukhala wachisoni,+

  • Yesaya 38:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Ine ndinati: “Pakatikati pa masiku anga ndidzalowa pazipata+ za Manda.

      Ndidzamanidwa zaka zanga zotsala.”+

  • Chivumbulutso 1:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena