Yobu 33:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Iye amayandikira kudzenje,+Ndipo moyo wake umayandikira kwa akupha. Yobu 38:17 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 17 Kodi anakuvundukulira zipata za imfa,+Kapena zipata za mdima wandiweyani,+ kodi ungathe kuziona? Salimo 9:13 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 13 Ndikomereni mtima inu Yehova. Onani mmene anthu odana nane akundisautsira,+Inu Mulungu amene mukundinyamula kundichotsa pazipata za imfa.+ Salimo 88:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pakuti ine ndakumana ndi masoka ochuluka,+Ndipo moyo wanga wayandikira ku Manda.+ Salimo 116:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Zingwe za imfa zinandizungulira+Ndipo ndinasautsika ngati kuti ndili m’Manda.+Ndinapitiriza kusautsika ndi kukhala wachisoni,+ Chivumbulutso 1:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+
13 Ndikomereni mtima inu Yehova. Onani mmene anthu odana nane akundisautsira,+Inu Mulungu amene mukundinyamula kundichotsa pazipata za imfa.+ Salimo 88:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Pakuti ine ndakumana ndi masoka ochuluka,+Ndipo moyo wanga wayandikira ku Manda.+ Salimo 116:3 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 3 Zingwe za imfa zinandizungulira+Ndipo ndinasautsika ngati kuti ndili m’Manda.+Ndinapitiriza kusautsika ndi kukhala wachisoni,+ Chivumbulutso 1:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+
3 Zingwe za imfa zinandizungulira+Ndipo ndinasautsika ngati kuti ndili m’Manda.+Ndinapitiriza kusautsika ndi kukhala wachisoni,+
18 ndiponso wamoyo.+ Ndinali wakufa,+ koma taona, ndili ndi moyo kwamuyaya,+ ndipo ndili ndi makiyi a imfa+ ndi a Manda.*+