Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  5 Mdima wandiweyani ulitenge.

      Mtambo wa mvula uliphimbe.

      Zinthu zimene zimadetsa tsiku ziliopseze.+

  • Yobu 38:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Kodi anakuvundukulira zipata za imfa,+

      Kapena zipata za mdima wandiweyani,+ kodi ungathe kuziona?

  • Salimo 23:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Ngakhale ndikuyenda m’chigwa cha mdima wandiweyani,+

      Sindikuopa kanthu,+

      Pakuti inu muli ndi ine.+

      Chibonga chanu ndi ndodo yanu ndi zimene zimandilimbikitsa.+

  • Salimo 88:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Kodi zodabwitsa zimene inu mukuchita zidzadziwika mu mdima?+

      Kapena kodi chilungamo chanu chidzadziwika m’dziko la anthu oiwalika?+

  • Mlaliki 9:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Chilichonse chimene dzanja lako lapeza kuti lichite, uchichite ndi mphamvu zako zonse,+ pakuti kulibe kugwira ntchito, kuganiza zochita, kudziwa zinthu,+ kapena nzeru,+ ku Manda*+ kumene ukupitako.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena