Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 4:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Upeze nzeru,+ upezenso luso lomvetsa zinthu.+ Usaiwale ndipo usapatuke pa mawu a m’kamwa mwanga.+

  • Miyambo 18:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Wodzipatula amafunafuna zolakalaka zake zosonyeza kudzikonda.+ Iye amachita zosemphana ndi nzeru zonse zopindulitsa.+

  • Luka 8:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Choncho muzimvetsera mwatcheru kwambiri. Pakuti amene ali nazo, adzapatsidwa zochuluka,+ koma amene alibe, adzalandidwa ngakhalenso zimene akuganizira kuti ali nazo.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena