Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Ekisodo 23:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 “Usapotoze chigamulo cha munthu wosauka wokhala pakati panu, pa mlandu wake.+

  • Yobu 29:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti ndinkapulumutsa wosautsika wopempha thandizo,+

      Ndiponso mwana wamasiye* ndi aliyense amene analibe womuthandiza.+

  • Amosi 5:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Pakuti ndadziwa kuchuluka kwa zochita zanu zondipandukira+ ndiponso kukula kwa machimo anu,+ inu amene mukuchitira nkhanza munthu wolungama,+ amene mukulandira ndalama za chitsekapakamwa+ ndiponso amene mukupondereza anthu osauka+ pachipata cha mzinda.+

  • Zekariya 7:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Musamabere mwachinyengo mkazi wamasiye,+ mwana wamasiye,*+ mlendo+ kapena munthu wosautsika.+ Musamakonzerane chiwembu mumtima mwanu.’+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena