Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 66:18
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 18 Ngati ndikuganizira choipa chilichonse mumtima mwanga,

      Yehova sadzandimvera.+

  • Salimo 109:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Pamene akuweruzidwa amuweruze kuti ndi woipa.

      Ndipo pemphero lake likhale tchimo.+

  • Miyambo 15:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Yehova amakhala kutali ndi anthu oipa,+ koma amamva pemphero la anthu olungama.+

  • Yesaya 1:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mukatambasula manja anu,+ ndimakubisirani maso anga.+ Ngakhale mupereke mapemphero ambiri,+ ine sindimvetsera.+ Manja anu adzaza magazi amene mwakhetsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena