Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 39:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 39 Ine ndinati: “Ndidzatchinjiriza njira zanga,+

      Kuti ndisachimwe ndi lilime langa.+

      Ndidzamanga pakamwa panga kuti patetezeke,+

      Nthawi zonse pamene woipa ali pamaso panga.”+

  • Miyambo 17:27
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 27 Aliyense wosalankhulapo mawu ake ndi wodziwa zinthu,+ ndipo munthu wozindikira amakhala wofatsa.+

  • Miyambo 21:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Wosunga pakamwa pake ndiponso lilime lake akuteteza moyo wake ku masautso.+

  • Yakobo 1:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Abale anga okondedwa, dziwani izi: Munthu aliyense akhale wofulumira kumva, wodekha polankhula,+ wosafulumira kukwiya,+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena