Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 141:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Inu Yehova, ikani mlonda pakamwa panga.+

      Ikani wolondera patsogolo pa milomo yanga.+

  • Miyambo 10:19
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 19 Pakachuluka mawu sipalephera kukhala zolakwa,+ koma wodziwa kulamulira milomo yake amachita zinthu mwanzeru.+

  • Miyambo 12:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Munthu woipa amakodwa ndi kuchimwa kwa milomo yake,+ koma wolungama amachoka m’masautso.+

  • Miyambo 13:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 3 Amene amayang’anira pakamwa pake amasunga moyo wake.+ Amene amatsegula kwambiri pakamwa pake adzawonongeka.+

  • Mlaliki 10:20
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 20 Ngakhale m’chipinda chako, usanenere mfumu zoipa,+ ndipo m’zipinda zimene umagona usanenere zoipa aliyense wolemera,+ chifukwa cholengedwa chouluka chikanena mawu ako ndipo chinachake chokhala ndi mapiko chikaulula zimene wanena.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena