Yoswa 2:14 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 14 Amunawo anayankha kuti: “Tikadzapanda kusunga lonjezo lathu, ifeyo tidzafe m’malo mwa inu!+ Mukasunga chinsinsi cha nkhaniyi, Yehova akadzatipatsa dziko lino, ifenso tidzakusonyezani kukoma mtima kosatha, ndipo tidzakhulupirika kwa inu.”+ Yoswa 2:20 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 20 Ndipo ngati ungaulule nkhaniyi,+ tidzakhalanso opanda mlandu pa pangano limene watilumbiritsali.” Yeremiya 38:27 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 27 Patapita nthawi, akalonga onse anafika kwa Yeremiya ndipo anayamba kumufunsa mafunso. Yeremiya anawayankha mogwirizana ndi mawu onsewa amene mfumu inamulamula.+ Choncho akalongawo anakhala chete pamaso pake chifukwa sanamve zimene anakambirana. Mateyu 1:19 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 19 Koma mwamuna wake Yosefe, pokhala munthu wolungama ndiponso posafuna kumuchititsa manyazi kwa anthu,+ anaganiza zomusiya+ mwamseri.*
14 Amunawo anayankha kuti: “Tikadzapanda kusunga lonjezo lathu, ifeyo tidzafe m’malo mwa inu!+ Mukasunga chinsinsi cha nkhaniyi, Yehova akadzatipatsa dziko lino, ifenso tidzakusonyezani kukoma mtima kosatha, ndipo tidzakhulupirika kwa inu.”+
27 Patapita nthawi, akalonga onse anafika kwa Yeremiya ndipo anayamba kumufunsa mafunso. Yeremiya anawayankha mogwirizana ndi mawu onsewa amene mfumu inamulamula.+ Choncho akalongawo anakhala chete pamaso pake chifukwa sanamve zimene anakambirana.
19 Koma mwamuna wake Yosefe, pokhala munthu wolungama ndiponso posafuna kumuchititsa manyazi kwa anthu,+ anaganiza zomusiya+ mwamseri.*