Genesis 39:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Potifara anapitiriza kumukonda Yosefe pamene anali kum’tumikira, moti anamusankha kukhala woyang’anira nyumba yake.+ Zonse zimene Potifara anali nazo anazipereka m’manja mwa Yosefe. 1 Mafumu 11:28 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 28 Yerobowamu anali mwamuna wamphamvu ndi wolimba mtima.+ Solomo ataona kuti mnyamatayo anali wogwira ntchito molimbika,+ anamuika kukhala woyang’anira+ ntchito yonse yokakamiza+ ya kunyumba ya Yosefe.+ Miyambo 17:2 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 2 Wantchito wochita zinthu mozindikira, adzalamulira mwana wa mbuye wake amene amachita zinthu zochititsa manyazi,+ ndipo adzalandira nawo cholowa pamodzi ndi ana a mbuye wake.+ Aheberi 6:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Koma tikufuna kuti aliyense wa inu apitirize kuonetsa khama limene anali nalo poyamba, kuti chiyembekezo+ chanu chikhale chotsimikizika+ mpaka mapeto.+
4 Potifara anapitiriza kumukonda Yosefe pamene anali kum’tumikira, moti anamusankha kukhala woyang’anira nyumba yake.+ Zonse zimene Potifara anali nazo anazipereka m’manja mwa Yosefe.
28 Yerobowamu anali mwamuna wamphamvu ndi wolimba mtima.+ Solomo ataona kuti mnyamatayo anali wogwira ntchito molimbika,+ anamuika kukhala woyang’anira+ ntchito yonse yokakamiza+ ya kunyumba ya Yosefe.+
2 Wantchito wochita zinthu mozindikira, adzalamulira mwana wa mbuye wake amene amachita zinthu zochititsa manyazi,+ ndipo adzalandira nawo cholowa pamodzi ndi ana a mbuye wake.+
11 Koma tikufuna kuti aliyense wa inu apitirize kuonetsa khama limene anali nalo poyamba, kuti chiyembekezo+ chanu chikhale chotsimikizika+ mpaka mapeto.+