Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 19:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 Zitatero Sauli anauza Mikala kuti: “N’chifukwa chiyani wandipusitsa+ chotere mwa kuthawitsa mdani wanga+ kuti apulumuke?” Poyankha, Mikala anauza Sauli kuti: “Iyeyo anandiuza kuti, ‘Ndilole ndipite! Apo ayi, ndikupha.’”

  • Nehemiya 6:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Iwo anamulemba ganyu+ n’cholinga choti ndichite mantha+ kuti ndikalowe m’kachisi ndi kuchimwa.+ Mwakutero, akanandiipitsira dzina langa+ kuti azindinyoza.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena