Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mbiri 29:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Ifetu ndife alendo pamaso panu, komanso okhala m’dziko la eni+ monga analili makolo athu onse. Masiku athu padziko lapansi ali ngati mthunzi,+ ndipo ndife osakhalitsa.

  • Yobu 8:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  9 Pakuti ife tabadwa dzulo,+ ndipo sitikudziwa kalikonse,

      Chifukwa masiku athu padziko lapansi ali ngati mthunzi.+

  • Yobu 14:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Amaphuka ngati duwa n’kuthotholedwa.+

      Amathawa ngati mthunzi+ ndipo sakhalaponso.

  • Salimo 102:11
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 11 Masiku a moyo wanga ali ngati chithunzithunzi chimene chimazimiririka dzuwa likalowa,+

      Ndipo ndauma ngati udzu.+

  • Salimo 144:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Munthu amafanana ndi mpweya wotuluka m’mphuno.+

      Masiku ake ali ngati mthunzi wongodutsa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena