Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Mafumu 10:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Odala anthu anu,+ odala+ atumiki anuwa amene amatumikira pamaso panu nthawi zonse, n’kumamva nzeru zanu.+

  • Yobu 4:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Aliyense wofuna kugwa, mawu ako anali kumudzutsa,+

      Ndipo mawondo olobodoka unali kuwachirikiza.+

  • Salimo 37:30
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 30 Pakamwa pa munthu wolungama pamalankhula zinthu zanzeru,+

      Ndipo lilime lake limalankhula zinthu zachilungamo.+

  • Miyambo 10:21
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 21 Milomo ya wolungama imaweta anthu ambiri,+ koma zitsiru zimafa chifukwa chopanda nzeru mumtima.+

  • Luka 4:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pamenepo onse anayamba kumutamanda ndi kudabwa ndi mawu ogwira mtima+ otuluka pakamwa pake, mwakuti anali kunena kuti: “Kodi iyeyu si mwana wa Yosefe?”+

  • Aefeso 4:29
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 29 Mawu alionse owola asatuluke pakamwa panu,+ koma alionse olimbikitsa monga mmene kungafunikire, kuti asangalatse owamva.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena