Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Miyambo 27:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 Mafuta ndi zofukiza zonunkhira+ n’zimene zimasangalatsa mtima, chimodzimodzinso kukoma kwa mnzako chifukwa cha malangizo ake ochokera pansi pa mtima, kumasangalatsa mtima.+

  • Mlaliki 9:8
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 8 Nthawi zonse zovala zako zizikhala zoyera,+ ndipo pamutu pako pasamasowe mafuta.+

  • Nyimbo ya Solomo 5:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Ine ndinadzuka kuti ndimutsegulire wachikondi wanga ndipo manja anga anali kuyenderera mafuta a mule. Zala zanga zinali kuyenderera mule pamene ndinali kugwira pabowo lolowetsapo loko wa pachitseko.

  • Luka 23:56
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 56 Atatero anabwerera kukakonza zonunkhiritsa ndi mafuta onunkhira.+ Komabe pa tsiku la sabata+ anapuma malinga ndi chilamulo.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena