Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • 1 Samueli 23:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Tsopano Yonatani mwana wa Sauli ananyamuka ndi kupita kwa Davide ku Horesi, kuti akalimbikitse+ Davide kudalira Mulungu.+

  • Miyambo 15:23
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 23 Munthu amasangalala ndi yankho lochokera pakamwa pake,+ ndipo mawu onenedwa pa nthawi yoyenera ndi abwino kwambiri.+

  • Miyambo 16:24
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 24 Mawu okoma ali ngati chisa cha uchi.+ Amakhala okoma kwa munthu ndipo amachiritsa mafupa.+

  • Machitidwe 28:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Abale akumeneko atamva za ife, anabwera kudzatichingamira ku Msika wa Apiyo ndi ku Nyumba Zitatu za Alendo. Paulo atawaona, anayamika Mulungu, ndipo analimba mtima.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena