Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Genesis 7:16
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 16 Zimene zinali kulowazo, zazimuna ndi zazikazi zamtundu uliwonse, zinalowa monga mmene Yehova anamulamulira Nowa. Kenako Yehova anatseka chitseko.+

  • Ekisodo 12:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Mukatero mutenge kamtengo ka hisope+ n’kukaviika m’beseni la magazi ndi kuwaza pafelemu la pamwamba pa chitseko, ndipo ena mwa magaziwo muwaze pamafelemu awiri a m’mbali mwa khomo. Aliyense asatuluke m’nyumba yake mpaka m’mawa.

  • Salimo 32:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Ndinu malo anga obisalamo, mudzanditeteza ku masautso.+

      Mudzachititsa kuti chisangalalo chindizungulire pamene mukundipulumutsa.+ [Seʹlah.]

  • Salimo 91:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+

      Udzathawira pansi pa mapiko ake.+

      Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.

  • Miyambo 18:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Dzina la Yehova ndi nsanja yolimba.+ Wolungama amathawira mmenemo ndipo amatetezedwa.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena