Ekisodo 19:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 ‘Inu munaona nokha zimene ndinachitira Aiguputo,+ kuti ndikunyamuleni pamapiko a chiwombankhanga ndi kukubweretsani kwa ine.+ Deuteronomo 32:11 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 11 Monga mmene chiwombankhanga chimagwedezera mwamphamvu chisa chake,Mmene chimaulukira pamwamba pa ana ake,+Mmene chimatambasulira mapiko ake, ndi kutenga anawo,N’kuwanyamula pamapiko ake,+ Salimo 91:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+Udzathawira pansi pa mapiko ake.+Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.
4 ‘Inu munaona nokha zimene ndinachitira Aiguputo,+ kuti ndikunyamuleni pamapiko a chiwombankhanga ndi kukubweretsani kwa ine.+
11 Monga mmene chiwombankhanga chimagwedezera mwamphamvu chisa chake,Mmene chimaulukira pamwamba pa ana ake,+Mmene chimatambasulira mapiko ake, ndi kutenga anawo,N’kuwanyamula pamapiko ake,+ Salimo 91:4 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+Udzathawira pansi pa mapiko ake.+Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.
4 Adzakutchinjiriza ndi mapiko ake,+Udzathawira pansi pa mapiko ake.+Choonadi chake+ chidzakhala chishango chako+ chachikulu ndi malo ako achitetezo.