Deuteronomo 28:66 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 66 Pamenepo moyo wako udzakhala pangozi yaikulu koopsa, ndipo udzakhala wamantha usiku ndi usana, moti sudzakhala wotsimikiza za moyo wako.+ Deuteronomo 28:67 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 67 M’mawa udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino akanakhala madzulo!’ ndipo madzulo udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino ukanakhala m’mawa!’ chifukwa cha mantha amene adzagwira mtima wako, ndiponso chifukwa cha zimene maso ako adzaona.+ Salimo 53:5 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 5 Nthawi yomweyo anagwidwa ndi mantha aakulu,+Ngakhale kuti panalibe chochititsa mantha.+Pakuti Mulungu adzamwaza mafupa a aliyense womanga msasa kuti akuukireni.+Isiraeli adzawachititsa manyazi pakuti Yehova wawakana.+
66 Pamenepo moyo wako udzakhala pangozi yaikulu koopsa, ndipo udzakhala wamantha usiku ndi usana, moti sudzakhala wotsimikiza za moyo wako.+
67 M’mawa udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino akanakhala madzulo!’ ndipo madzulo udzanena kuti, ‘Zikanakhala bwino ukanakhala m’mawa!’ chifukwa cha mantha amene adzagwira mtima wako, ndiponso chifukwa cha zimene maso ako adzaona.+
5 Nthawi yomweyo anagwidwa ndi mantha aakulu,+Ngakhale kuti panalibe chochititsa mantha.+Pakuti Mulungu adzamwaza mafupa a aliyense womanga msasa kuti akuukireni.+Isiraeli adzawachititsa manyazi pakuti Yehova wawakana.+