Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 44:4
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  4 Inu Mulungu, ndinu Mfumu yanga.+

      Lamulani kuti Yakobo alandire chipulumutso chachikulu.+

  • Salimo 74:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Koma Mulungu ndi Mfumu yanga kuyambira kalekale,+

      Iye ndiye wondipatsa chipulumutso chachikulu padziko lapansi.+

  • Salimo 97:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 97 Yehova wakhala mfumu!+ Dziko lapansi likondwere,+

      Ndipo zilumba zambiri zisangalale.+

  • Chivumbulutso 11:17
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 17 ndi mawu akuti: “Tikukuyamikani+ inu Yehova, Mulungu Wamphamvuyonse,+ Inu amene mulipo+ ndi amene munalipo, chifukwa mwatenga mphamvu yanu yaikulu+ ndi kuyamba kulamulira monga mfumu.+

  • Chivumbulutso 19:6
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 6 Kenako ndinamva mawu ngati a khamu lalikulu, omveka ngati mkokomo wa madzi ambiri ndi mabingu amphamvu. Mawuwo anati: “Tamandani Ya,+ anthu inu, chifukwa Yehova* Mulungu wathu, Wamphamvuyonse,+ wayamba kulamulira monga mfumu.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena