Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Salimo 97:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 97 Yehova wakhala mfumu!+ Dziko lapansi likondwere,+

      Ndipo zilumba zambiri zisangalale.+

  • Yesaya 52:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 Mapazi+ a munthu yemwe akuyenda pamwamba pa mapiri pobweretsa uthenga wabwino, ndi okongola kwabasi!+ Munthu yemwe akulengeza za mtendere,+ yemwe akubweretsa uthenga wabwino wa zinthu zabwino kuposa kale,+ yemwe akulengeza za chipulumutso,+ yemwe akuuza Ziyoni kuti: “Mulungu wako wakhala mfumu.”+

  • Danieli 7:9
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 9 “Ndiyeno ndinapitiriza kuyang’ana kufikira pamene mipando yachifumu inaikidwa+ ndipo Wamasiku Ambiri+ anakhala pa mpando wake wachifumu. Zovala zake zinali zoyera kwambiri.+ Tsitsi lake linali looneka ngati ubweya wa nkhosa woyera.+ Mpando wake wachifumu unali kuyaka moto walawilawi,+ ndipo mawilo a mpandowo anali kuyaka moto.+

  • Chivumbulutso 11:15
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 15 Mngelo wa 7 analiza lipenga+ lake. Ndipo kumwamba kunamveka mawu osiyanasiyana, akunena mokweza kuti: “Ufumu wa dziko wakhala ufumu wa Ambuye wathu+ ndi wa Khristu wake.+ Iye adzalamulira monga mfumu kwamuyaya.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena