Yesaya 29:18 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 18 M’tsiku limenelo, ogontha adzamva mawu a m’buku.+ Ngakhale maso a anthu akhungu adzamasuka ku mdima wandiweyani ndipo adzayamba kuona.+ Yeremiya 6:10 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 10 “Kodi ndilankhule ndi ndani ndipo ndichenjeze ndani kuti amve? Taonani! Makutu awo sanawachite mdulidwe, moti sangamve.+ Taonani! Mawu a Yehova akhala onyozeka kwa iwo,+ ndipo sakukondwera nawo.+ Maliko 7:35 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 35 Atatero, makutu ake anatseguka,+ lilime lake lomangikalo linamasuka, moti anayamba kulankhula bwinobwino. Luka 7:22 Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika 22 Choncho poyankha anauza amuna awiri aja kuti: “Pitani+ mukamuuze Yohane zimene mwaona ndi kumva: Akhungu+ akuona, olumala akuyenda, akhate akuyeretsedwa, ogontha akumva, akufa akuukitsidwa ndipo aumphawi akumva+ uthenga wabwino.+
18 M’tsiku limenelo, ogontha adzamva mawu a m’buku.+ Ngakhale maso a anthu akhungu adzamasuka ku mdima wandiweyani ndipo adzayamba kuona.+
10 “Kodi ndilankhule ndi ndani ndipo ndichenjeze ndani kuti amve? Taonani! Makutu awo sanawachite mdulidwe, moti sangamve.+ Taonani! Mawu a Yehova akhala onyozeka kwa iwo,+ ndipo sakukondwera nawo.+
35 Atatero, makutu ake anatseguka,+ lilime lake lomangikalo linamasuka, moti anayamba kulankhula bwinobwino.
22 Choncho poyankha anauza amuna awiri aja kuti: “Pitani+ mukamuuze Yohane zimene mwaona ndi kumva: Akhungu+ akuona, olumala akuyenda, akhate akuyeretsedwa, ogontha akumva, akufa akuukitsidwa ndipo aumphawi akumva+ uthenga wabwino.+