-
2 Mafumu 19:23Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
-
-
23 Kudzera mwa amithenga ako+ watonza Yehova ndipo wanena kuti,+
‘Ndi magaleta anga ankhondo ambiri, ine,+
Ineyo ndidzakwera ndithu madera amapiri mpaka pamwamba.+
Ndidzafika kumadera akutali kwambiri a Lebanoni+
Ndipo ndidzadula mitengo yake ya mkungudza+ italiitali, ndi mitengo yake yabwino kwambiri yofanana ndi mkungudza.+
Ndidzalowa kumalo ake okhala akutali kwambiri, kunkhalango yokongola.+
-