Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 2:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kenako anakhala+ naye limodzi pansi masiku 7 usana ndi usiku, ndipo palibe amene anali kumulankhula chilichonse popeza iwo anaona kuti ululu+ wake unali waukulu kwambiri.

  • Yesaya 47:1
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 47 Tsika ukhale pansi pafumbi+ iwe namwali, mwana wamkazi wa Babulo.+ Khala padothi pomwe palibe mpando wachifumu,+ iwe mwana wamkazi wa Akasidi.+ Pakuti anthu adzaleka kukutchula kuti ndiwe wolekereredwa ndiponso wosasatitsidwa.*+

  • Maliro 2:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Akuluakulu a mwana wamkazi wa Ziyoni akhala pansi ndipo akhala chete.+

      Iwo athira fumbi pamitu+ yawo ndipo avala ziguduli.*+

      Anamwali a Yerusalemu aweramitsa mitu yawo mpaka padothi.+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena