Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yobu 26:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  7 Iye anatambasula kumpoto pamwamba pa malo opanda kanthu,+

      Ndipo anakoloweka dziko lapansi m’malere.

  • Salimo 104:2
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  2 Mwadzifunditsa kuwala ngati chofunda,+

      Mwatambasula kumwamba ngati nsalu ya chihema.+

  • Yesaya 40:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Pali Winawake amene amakhala pamwamba pa dziko lapansi lozungulira,+ limene okhalamo ake ali ngati ziwala. Iye anayala kumwamba ngati nsalu yopyapyala, ndipo anakutambasula ngati hema wokhalamo.+

  • Yesaya 45:12
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 12 Ineyo ndinapanga dziko lapansi+ ndipo ndinalenga munthu n’kumuikapo.+ Manja anga anatambasula kumwamba,+ ndipo nyenyezi ndi zonse zimene zili kumwambako ndimazilamulira.”+

  • Yesaya 51:13
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 13 Kodi n’chifukwa chiyani ukuiwala Yehova amene anakupanga,+ amene anatambasula kumwamba+ ndi kuyala maziko a dziko lapansi?+ N’chifukwa chiyani ukuchita mantha nthawi zonse, tsiku lonse lathunthu, poopa mkwiyo wa yemwe akukupanikizira mkati,+ ngati kuti iye wakonzeka kuti akuwononge?+ Kodi mkwiyo wa amene akukupanikizira mkati uli kuti?+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena