Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Yeremiya 13:22
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 22 Ukadzanena mumtima mwako kuti,+ ‘N’chifukwa chiyani zinthu zimenezi zandigwera?’+ pamenepo udzadziwe kuti wavulidwa siketi yako+ ndipo zidendene zako zazunzidwa chifukwa zolakwa zako zachuluka.

  • Nahumu 3:5
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 5 Yehova wa makamu wanena kuti: “Taona! Ine ndikukuukira,+ ndipo ndidzakuvula siketi yako ndi kukuphimba nayo kumaso moti ndidzachititsa kuti mitundu ya anthu ione maliseche ako+ ndi kutinso maufumu aone manyazi ako.

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena