Watchtower LAIBULALE YA PA INTANETI
Watchtower
LAIBULALE YA PA INTANETI
Chichewa
  • BAIBULO
  • MABUKU
  • MISONKHANO
  • Deuteronomo 9:7
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 7 “Kumbukirani izi: Simuyenera kuiwala mmene munaputira Yehova Mulungu wanu m’chipululu.+ Anthu inu mwasonyeza khalidwe lopandukira Yehova kuyambira tsiku limene munatuluka m’dziko la Iguputo mpaka kudzafika malo ano.+

  • Salimo 58:3
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    •  3 Oipa akhala opotoka maganizo kuyambira ali m’mimba.+

      Iwo asochera kuyambira ali m’mimba,

      Ndipo amalankhula zabodza.+

  • Salimo 95:10
    Baibulo la Dziko Latsopano la Malemba Opatulika
    • 10 Kwa zaka 40, m’badwo umenewo unali kundinyansa,+

      Ndipo ndinati:

      “Anthu awa mitima yawo imasochera,+

      Ndipo sadziwa njira zanga.”+

Mabuku a Chichewa (1974-2025)
Tulukani
Lowani
  • Chichewa
  • Tumizirani Ena
  • Zimene Mumakonda
  • Copyright © 2025 Watch Tower Bible and Tract Society of Pennsylvania
  • Zoyenera Kutsatira
  • Nkhani Yosunga Chinsinsi
  • Privacy Settings
  • JW.ORG
  • Lowani
Tumizirani Ena